Masalimo 70:3 - Buku Lopatulika3 Abwerere, kukhale mphotho ya manyazi ao amene akuti, Hede, hede. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Abwerere, kukhale mphotho ya manyazi ao amene akuti, Hede, hede. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Amene amandinyodola kuti, “Ha, Ha,” achoke ndi manyazi poona kuti alephera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo. Onani mutuwo |