Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 70:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Abwerere, kukhale mphotho ya manyazi ao amene akuti, Hede, hede.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Abwerere, kukhale mphotho ya manyazi ao amene akuti, Hede, hede.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Amene amandinyodola kuti, “Ha, Ha,” achoke ndi manyazi poona kuti alephera.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 70:3
10 Mawu Ofanana  

Iwo amandiseka mofuwula ndipo amati, “Haa! Haa! Ndipo ndi maso athuwa ife taziona.”


Musalole kuti aganize kuti, “Amati atani, zachitika monga momwe timafunira!” Kapena kunena kuti, “Tamutha ameneyu basi.”


Iwo amene amanena kwa ine kuti, “Hee! Hee!” abwerere akuchita manyazi.


Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi, iwo amene akufuna kundipweteka avale chitonzo ndi manyazi.


Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo tsiku lonse, pakuti iwo amene amafuna kundipweteka achititsidwa manyazi ndi kusokonezedwa.


Awawuze kuti, ‘Inu anthu a ku Amoni, imvani zimene Ambuye Yehova akunena. Iye akuti: Inu munanena mawu onyoza pamene Nyumba yanga yopatulika inkayipitsidwa. Munanyozanso dziko la Israeli pamene linaguga ndiponso anthu a ku Yuda pamene anatengedwa ukapolo.


“Iwe mwana wa munthu, anthu a ku Turo ananyogodola Yerusalemu kuti ‘Hii! Uja amene anali chipata choloweramo anthu a mitundu ina wawonongeka. Zitseko zake zatsekukira ife. Tidzalemera popeza wasanduka bwinja.’


Ine Ambuye Yehova ndikuti: Mdani wanu ankanena kuti, ‘Aa! Dziko lamapiri lakalekale lija lasanduka lathu.’


(Yudasi anagula munda ndi ndalama zimene anazipeza pochita zoyipa zija; kumeneko, iye anagwa chamutu, naphulika pakati ndipo matumbo ake wonse anakhuthuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa