Masalimo 6:3 - Buku Lopatulika3 Moyo wanganso wanthunthumira kwakukulu; ndipo Inu, Yehova, kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Moyo wanganso wanthunthumira kwakukulu; ndipo Inu, Yehova, kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mtima wanganso wazunzika kwambiri. Nanga Inu Chauta, zimenezi zidzakhala zikuchitika mpaka liti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu. Mpaka liti, Inu Yehova, mpaka liti? Onani mutuwo |