Masalimo 4:2 - Buku Lopatulika2 Amuna inu, ulemu wanga udzakhala wamanyazi kufikira liti? Mudzakonda zachabe, ndi kufunafuna bodza kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Amuna inu, ulemu wanga udzakhala wamanyazi kufikira liti? Mudzakonda zachabe, ndi kufunafuna bodza kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu inu, mudzaleka liti kunyoza ulemu wanga? Bwanji mukukondabe zinthu zachabechabe? Bwanji mukulakalakabe zinthu zonama? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? Sela. Onani mutuwo |