Masalimo 3:7 - Buku Lopatulika7 Ukani Yehova; ndipulumutseni, Mulungu wanga! Pakuti mwapanda adani anga onse patsaya; mwawathyola mano oipawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ukani Yehova; ndipulumutseni, Mulungu wanga! Pakuti mwapanda adani anga onse patsaya; mwawathyola mano oipawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu Chauta, dzambatukani, mundipulumutse Inu Mulungu wanga. Adani anga onse mwaŵaomba makofi, anthu oipa mwaŵagulula mano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Dzukani, Inu Yehova! Pulumutseni, Inu Mulungu wanga. Akantheni adani anga onse pa msagwada; gululani mano a anthu oyipa. Onani mutuwo |