Masalimo 3:5 - Buku Lopatulika5 Ndinagona ine pansi, ndinagona tulo; ndinauka; pakuti Yehova anandichirikiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndinagona ine pansi, ndinagona tulo; ndinauka; pakuti Yehova anandichirikiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndimagona ndipo ndimapeza tulo. Ndimadzukanso m'maŵa pakuti Chauta amanditchinjiriza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo; ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza. Onani mutuwo |