Masalimo 3:4 - Buku Lopatulika4 Ndifuula kwa Yehova ndi mau anga, ndipo andiyankha m'phiri lake loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndifuula kwa Yehova ndi mau anga, ndipo andiyankha m'phiri lake loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndimafuulira Chauta kuti andithandize, Iye amandiyankha ali pa phiri lake loyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera. Sela Onani mutuwo |