Masalimo 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndidzauza za chitsimikizo: Yehova ananena ndi Ine, Iwe ndiwe Mwana wanga; Ine lero ndakubala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndidzauza za chitsimikizo: Yehova ananena ndi Ine, Iwe ndiwe Mwana wanga; Ine lero ndakubala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono mfumuyo ikuti, “Ndidzalalika zimene Chauta walengeza. Adandiwuza kuti, ‘Iwe ndiwe mwana wanga, Ine lero ndakubala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako. Onani mutuwo |