Masalimo 148:8 - Buku Lopatulika8 moto ndi matalala, chipale chofewa ndi nkhungu; mphepo ya namondwe, yakuchita mau ake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 moto ndi matalala, chipale chofewa ndi nkhungu; mphepo ya namondwe, yakuchita mau ake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 inu moto ndi matalala, inu chisanu chambee ndi mitambo, inu mphepo zamkuntho, okwaniritsa zolamula Chauta! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 inu zingʼaningʼani ndi matalala, chipale ndi mitambo, mphepo yamkuntho imene imakwaniritsa mawu ake, Onani mutuwo |