Masalimo 146:5 - Buku Lopatulika5 Wodala munthu amene akhala naye Mulungu wa Yakobo kuti amthandize, chiyembekezo chake chili pa Yehova, Mulungu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wodala munthu amene akhala naye Mulungu wa Yakobo kuti amthandize, chiyembekezo chake chili pa Yehova, Mulungu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ngwodala munthu amene chithandizo chake chimafumira kwa Mulungu wa Yakobe, munthu amene amakhulupirira Chauta, Mulungu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Wodala ndi amene thandizo lake ndi Mulungu wa Yakobo. Onani mutuwo |