Masalimo 114:3 - Buku Lopatulika3 Nyanjayo inaona, nithawa; Yordani anabwerera m'mbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nyanjayo inaona, nithawa; Yordani anabwerera m'mbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nyanja idaona zimenezi nithaŵa, mtsinje wa Yordani udabwerera m'mbuyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo; Onani mutuwo |