Masalimo 114:2 - Buku Lopatulika2 Yuda anakhala malo ake oyera, Israele ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yuda anakhala malo ake oyera, Israele ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Yuda adasanduka malo opatulika a Chauta, Aisraele adasanduka anthu a mu ufumu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake. Onani mutuwo |