Masalimo 114:1 - Buku Lopatulika1 M'mene Israele anatuluka ku Ejipito, nyumba ya Yakobo kwa anthu a chinenedwe chachilendo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 M'mene Israele anatuluka ku Ejipito, nyumba ya Yakobo kwa anthu a chinenedwe chachilendo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Israele adatuluka ku Ejipito, pamene banja la Yakobe lidatuluka kuchokera ku mtundu wa anthu a chilankhulo chachilendo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo, Onani mutuwo |