2 Samueli 22:8 - Buku Lopatulika8 Pomwepo dziko linagwedezeka ndi kunthunthumira. Maziko a dziko la kumwamba anasunthika. Nagwedezeka, chifukwa Iye anakwiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pomwepo dziko linagwedezeka ndi kunthunthumira. Maziko a dziko la kumwamba anasunthika. Nagwedezeka, chifukwa Iye anakwiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Pamenepo dziko lapansi lidanjenjemera ndi kuchita chivomezi. Maziko akumwamba adagwedezeka ndi kulilima chifukwa Chauta adaakalipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Dziko lapansi linanjenjemera ndi kuchita chivomerezi, maziko a miyamba anagwedezeka; ananjenjemera chifukwa Iye anakwiya. Onani mutuwo |