2 Samueli 22:9 - Buku Lopatulika9 M'mphuno mwake munatuluka utsi, ndi moto wotuluka m'kamwa mwake unaononga; makala anayaka nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 M'mphuno mwake munatuluka utsi, ndi moto wotuluka m'kamwa mwake unaononga; makala anayaka nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 M'mphuno mwake munkafuka utsi, m'kamwa mwake munkatuluka moto woononga, makala amoto anali laŵilaŵi kuchokera m'kamwa momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mʼmphuno mwake munatuluka utsi; moto wonyeketsa unatuluka mʼkamwa mwake, makala amoto anali lawilawi mʼkamwa mwake. Onani mutuwo |