Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 2:3 - Buku Lopatulika

Ndipo taonani, mthenga wolankhula nane anatuluka, ndi mthenga wina anatuluka kukomana naye,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo taonani, mthenga wolankhula nane anatuluka, ndi mthenga wina anatuluka kukomana naye,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo mngelo uja ankalankhula naneyu adasendera, mngelo winanso adadzakumana naye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Taonani, mngelo amene amayankhula nane uja akuchoka, mngelo wina anabwera kudzakumana naye

Onani mutuwo



Zekariya 2:3
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinati kwa mthenga wakulankhula ndi ine, Izi nziyani? Ndipo anandiyankha, Izi ndi nyangazi zinabalalitsa Yuda, Israele, ndi Yerusalemu.


nanena naye, Thamanga, lankhula ndi mnyamata uyu, ndi kuti, Mu Yerusalemu mudzakhala anthu ngati m'midzi yopanda malinga, chifukwa cha kuchuluka anthu ndi zoweta momwemo.


Ndipo mthengayo adalankhula nane, anadzanso, nandiutsa ngati munthu woutsidwa m'tulo take.


Ndipo mthenga wakulankhula ndi ine anayankha, nati kwa ine, Sudziwa kodi kuti nziyani izi? Ndipo ndinati, Iai, mbuyanga.


Pamenepo mthenga wakulankhula ndi ine anatuluka, nati kwa ine, Kwezatu maso ako, nuone ngati nchiyani ichi chilikutulukachi.