Zekariya 5:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo mthenga wakulankhula ndi ine anatuluka, nati kwa ine, Kwezatu maso ako, nuone ngati nchiyani ichi chilikutulukachi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo mthenga wakulankhula ndi ine anatuluka, nati kwa ine, Kwezatu maso ako, nuone ngati nchiyani ichi chilikutulukachi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pambuyo pake mngelo amene ankalankhula nane uja adabwera, nandiwuza kuti, “Upenyetsetse, uwone chinthu chikubwerachi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kenaka mngelo amene amayankhula nane uja anabwera patsogolo panga ndipo anandiwuza kuti, “Kweza maso ako tsopano kuti uwone kuti ndi chiyani chikubwerachi.” Onani mutuwo |