Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 2:9 - Buku Lopatulika

Alumphira mzinda, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati khungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Alumphira mudzi, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati khungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akuulumphira mzindawo, akukwera pamwamba pa malinga. Akuloŵa m'nyumba, akuloŵera pa windo ngati mbala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amakhamukira mu mzinda, amathamanga mʼmbali mwa khoma. Amakwera nyumba ndi kulowamo; amalowera pa zenera ngati mbala.

Onani mutuwo



Yoweli 2:9
5 Mawu Ofanana  

Ndipo dzombe linakwera padziko lonse la Ejipito, ndipo linatera pakati pa malire onse Ejipito, lambirimbiri; lisanafike ili panalibe dzombe lotere longa ili, ndipo litapita ili sipadzakhalanso lotere.


ndipo lidzadzaza m'nyumba zako, ndi m'nyumba za anyamata ako onse, ndi m'nyumba za Aejipito onse; sanachione chotere atate ako kapena makolo ako, kuyambira tsiku lija lakukhala iwo padziko lapansi kufikira lero lino. Ndipo anatembenuka, natuluka kwa Farao.


Pakuti imfa yakwera m'mazenera athu, yalowa m'nyumba mwathu; kuchotsa ana kubwalo, ndi anyamata kumiseu.


Sakankhana, ayenda lililonse m'mopita mwake; akagwa m'zida, siithyoka nkhondo yao.


Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Iye wosalowa m'khola la nkhosa pakhomo, koma akwerera kwina, iyeyu ndiye wakuba ndi wolanda.