Yeremiya 9:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti imfa yakwera m'mazenera athu, yalowa m'nyumba mwathu; kuchotsa ana kubwalo, ndi anyamata kumiseu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti imfa yakwera m'mazenera athu, yalowa m'nyumba mwathu; kuchotsa ana kubwalo, ndi anyamata kumiseu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Imfa yatifikira kudzera m'mawindo, yaloŵa ngakhale m'nyumba zathu zaufumu. Idapha ana athu m'miseu, ndipo idatha anyamata m'mabwalo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Imfa yatifikira kudzera mʼmazenera athu ndipo yalowa mʼnyumba zathu zotetezedwa; yapha ana athu mʼmisewu, ndi achinyamata athu mʼmabwalo. Onani mutuwo |