Yoweli 2:10 - Buku Lopatulika10 Dziko lapansi linjenjemera pamaso pao, thambo ligwedezeka, dzuwa ndi mwezi zada, ndi nyenyezi zibweza kuwala kwao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Dziko lapansi linjenjemera pamaso pao, thambo ligwedezeka, dzuwa ndi mwezi zada, ndi nyenyezi zibweza kuwala kwao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Dziko lapansi likugwedezeka pamene iwo akuyandikira. Mlengalenga ukunjenjemera. Dzuŵa ndi mwezi zikuchita mdima, ndipo nyenyezi zikuleka kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Patsogolo pawo dziko limagwedezeka, thambo limanjenjemera, dzuwa ndi mwezi zimachita mdima, ndipo nyenyezi zimaleka kuwala. Onani mutuwo |