Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoweli 2:9 - Buku Lopatulika

9 Alumphira mzinda, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati khungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Alumphira mudzi, athamanga palinga, akwerera nyumba, alowera pamazenera ngati khungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Akuulumphira mzindawo, akukwera pamwamba pa malinga. Akuloŵa m'nyumba, akuloŵera pa windo ngati mbala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Amakhamukira mu mzinda, amathamanga mʼmbali mwa khoma. Amakwera nyumba ndi kulowamo; amalowera pa zenera ngati mbala.

Onani mutuwo Koperani




Yoweli 2:9
5 Mawu Ofanana  

Ndipo dzombe linakwera padziko lonse la Ejipito, ndipo linatera pakati pa malire onse Ejipito, lambirimbiri; lisanafike ili panalibe dzombe lotere longa ili, ndipo litapita ili sipadzakhalanso lotere.


ndipo lidzadzaza m'nyumba zako, ndi m'nyumba za anyamata ako onse, ndi m'nyumba za Aejipito onse; sanachione chotere atate ako kapena makolo ako, kuyambira tsiku lija lakukhala iwo padziko lapansi kufikira lero lino. Ndipo anatembenuka, natuluka kwa Farao.


Pakuti imfa yakwera m'mazenera athu, yalowa m'nyumba mwathu; kuchotsa ana kubwalo, ndi anyamata kumiseu.


Sakankhana, ayenda lililonse m'mopita mwake; akagwa m'zida, siithyoka nkhondo yao.


Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Iye wosalowa m'khola la nkhosa pakhomo, koma akwerera kwina, iyeyu ndiye wakuba ndi wolanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa