Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 3:7 - Buku Lopatulika

Usadabwe chifukwa ndinati kwa iwe, Uyenera kubadwa mwatsopano.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Usadabwe chifukwa ndinati kwa iwe, Uyenera kubadwa mwatsopano.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Usadabwe m'mene ndakuuza kuti muyenera kubadwanso.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwe usadabwe chifukwa ndakuwuza kuti, ‘Uyenera kubadwanso.’

Onani mutuwo



Yohane 3:7
17 Mawu Ofanana  

Munthu nchiyani kuti akhale woyera, wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama?


Ngati ndakuuzani za pansi pano, ndipo simukhulupirira, mudzakhulupirira bwanji, ngati ndikuuzani za Kumwamba?


Yesu anayankha nati kwa iye, Indetu, indetu, ndinena ndi iwe, Ngati munthu sabadwa mwatsopano, sangathe kuona Ufumu wa Mulungu.


Chobadwa m'thupi chikhala thupi, ndipo chobadwa mwa Mzimu, chikhala mzimu.


Mphepo iomba pomwe ifuna, ndipo ukumva mau ake, koma sudziwa kumene ichokera, ndi kumene imuka; chotero aliyense wobadwa mwa Mzimu.


Musazizwe ndi ichi, kuti ikudza nthawi, imene onse ali m'manda adzamva mau ake,


ndi kuyamika Atate, amene anatiyeneretsa ife kulandirana nao cholowa cha oyera mtima m'kuunika;


Londolani mtendere ndi anthu onse, ndi chiyeretso chimene, akapanda ichi, palibe mmodzi adzaona Ambuye:


Popeza mwayeretsa moyo wanu pakumvera choonadi kuti mukakonde abale ndi chikondi chosanyenga, mukondane kwenikweni kuchokera kumtima;


ndipo simudzalowa konse momwemo kanthu kalikonse kosapatulidwa kapena iye wakuchita chonyansa ndi bodza; koma iwo okha olembedwa m'buku la moyo la Mwanawankhosa.