Akolose 1:12 - Buku Lopatulika12 ndi kuyamika Atate, amene anatiyeneretsa ife kulandirana nao cholowa cha oyera mtima m'kuunika; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndi kuyamika Atate, amene anatiyeneretsa ife kulandirana nao cholowa cha oyera mtima m'kuunika; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo timapemphera kuti muziyamika Atate, amene adakuyenerezani kuti mudzalandire nao madalitso onse amene amasungira anthu ao mu ufumu wa kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 ndi kuyamika Atate nthawi zonse, amene wakuyenerezani kuti mulandire nawo chuma cha oyera mtima mu ufumu wa kuwunika. Onani mutuwo |