Akolose 1:13 - Buku Lopatulika13 amene anatilanditsa ife kuulamuliro wa mdima, natisunthitsa kutilowetsa mu ufumu wa Mwana wa chikondi chake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 amene anatilanditsa ife kuulamuliro wa mdima, natisunthitsa kutilowetsa m'ufumu wa Mwana wa chikondi chake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adatilanditsa ku mphamvu za mdima wa zoipa, nkutiloŵetsa mu Ufumu wa Mwana wake wokondedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti Iye anatipulumutsa ku ulamuliro wa mdima ndi kutibweretsa mu ufumu wa Mwana wake wokondedwa. Onani mutuwo |