Yohane 5:28 - Buku Lopatulika28 Musazizwe ndi ichi, kuti ikudza nthawi, imene onse ali m'manda adzamva mau ake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Musazizwe ndi ichi, kuti ikudza nthawi, imene onse ali m'manda adzamva mau ake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Musadabwe nazo zimenezi, pakuti ikudza nthaŵi pamene anthu onse amene ali m'manda adzamva mau ake nadzatuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “Musadabwe ndi zimenezi. Pakuti nthawi ikubwera pamene onse amene ali mʼmanda adzamva mawu ake Onani mutuwo |