Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 3:1 - Buku Lopatulika

Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wina wa m'gulu la Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo panali Mfarisi wotchedwa Nekodimo, wa mʼgulu lolamulira la Ayuda.

Onani mutuwo



Yohane 3:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,


Koma anadzanso Nikodemo, amene anadza kwa Iye usiku poyamba paja, alikutenga chisakanizo cha mure ndi aloe, monga miyeso zana.


Yesu anayankha nati kwa iye, Kodi uli mphunzitsi wa Israele, ndipo sudziwa izi?


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?