Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pilato adasonkhanitsa akulu a ansembe ndi akulu a Ayuda ndi anthu wamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pilato anasonkhanitsa akulu a ansembe, oweruza ndi anthu,

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:13
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Pilato ananena nao, Pakuti Iye anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsatu, Mpachikeni Iye.


Ndipo anthu anaima alikupenya. Ndi akulunso anamlalatira Iye, nanena, Anapulumutsa ena; adzipulumutse yekha ngati iye ndiye Khristu wa Mulungu, wosankhidwa wake.


ndi kuti ansembe aakulu ndi akulu athu anampereka Iye ku chiweruziro cha imfa, nampachika Iye pamtanda.


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Pilato ananena kwa Iye, Choonadi nchiyani? Ndipo pamene adanena ichi, anatulukiranso kwa Ayudawo, nanena nao, Ine sindipeza konse chifukwa mwa Iye.


Ndipo Pilato anatulukanso kunja, nanena nao, Taonani, ndidza naye kwa inu kunja kuti mudziwe kuti sindipeza mwa Iye chifukwa chilichonse.


Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?


Kodi wina wa akulu anakhulupirira Iye, kapena wa Afarisi?


Pakuti iwo akukhala mu Yerusalemu, ndi akulu ao, popeza sanamzindikire Iye, ngakhale mau a aneneri owerengedwa masabata onse, anawakwaniritsa pakumtsutsa.


Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munachichita mosadziwa, monganso akulu anu.


Koma panali m'mawa mwake, anasonkhana pamodzi mu Yerusalemu oweruza, ndi akulu, ndi alembi;


Pamenepo Petro, wodzala ndi Mzimu Woyera anati kwa iwo, Oweruza a anthu inu, ndi akulu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa