Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Herode ndi Pilato anachitana chibwenzi tsiku lomwelo; pakuti kale anadana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Herode ndi Pilato anachitana chibwenzi tsiku lomwelo; pakuti kale anadana.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsiku lomwelo Herode ndi Pilato adayamba kuyanjana, chonsecho kale ankadana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Tsiku limenelo, Herode ndi Pilato anakhala abwenzi. Zisanachitike izi anali adani.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi ndi Asaduki anadza, namuyesa, namfunsa Iye awaonetse chizindikiro cha Kumwamba.


ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo.


Pakuti zoonadi anasonkhanidwa m'mzinda muno Herode, ndi Pontio Pilato yemwe pamodzi ndi amitundu ndi anthu a Israele kumchitira choipa Mwana wanu wopatulika Yesu amene munamdzoza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa