Luka 23:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Herode ndi asilikali ake anampeputsa Iye, namnyoza, namveka Iye chofunda chonyezimira, nambwezera kwa Pilato. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Herode ndi asilikali ake anampeputsa Iye, namnyoza, namveka Iye chofunda chonyezimira, nambwezera kwa Pilato. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Herode pamodzi ndi asilikali ake adayamba kumseka Yesu ndi kumamnyoza. Adamuveka chovala chachifumu, namubwezera kwa Pilato. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamenepo Herode ndi asilikali ake anamuseka ndi kumunyoza Iye. Atamuveka mkanjo wonyezimira, anamutumizanso kwa Pilato. Onani mutuwo |