Yohane 19:39 - Buku Lopatulika39 Koma anadzanso Nikodemo, amene anadza kwa Iye usiku poyamba paja, alikutenga chisakanizo cha mure ndi aloe, monga miyeso zana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Koma anadzanso Nikodemo, amene anadza kwa Iye usiku poyamba paja, alikutenga chisanganizo cha mure ndi aloe, monga miyeso zana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Kudabweranso Nikodemo, yemwe uja amene adaabwera kwa Yesu usiku poyamba paja. Iye adabwera ndi mafuta onunkhira a mure osanganiza ndi aloe, kulemera kwake ngati makilogaramu 32. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Nekodimo, munthu amene poyamba pake anabwera kwa Yesu usiku, anatenga mafuta osakaniza ndi mure ndi aloe wolemera pafupifupi makilogalamu 32. Onani mutuwo |