Yohane 2:25 - Buku Lopatulika25 ndipo sanasowe wina achite umboni za munthu; pakuti anadziwa Iye yekha chimene chinali mwa munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 ndipo sanasowe wina achite umboni za munthu; pakuti anadziwa Iye yekha chimene chinali mwa munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Sankalira kuti wina achite chomuuza za munthu aliyense. Pakuti mwiniwakeyo ankadziŵa za m'mitima mwa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iye sanafune umboni wa wina aliyense popeza amadziwa zomwe zinali mʼmitima mwa anthu. Onani mutuwo |