Yohane 2:24 - Buku Lopatulika24 Koma Yesu sanakhulupirire iwo kuti akhale nao, chifukwa Iye anadziwa anthu onse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma Yesu sanakhulupirire iwo kuti akhale nao, chifukwa Iye anadziwa anthu onse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma Yesu sadaikepo chikhulupiriro pa iwowo, popeza kuti Iye ankaŵadziŵa anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Yesu sanawakhulupirire iwo, pakuti amadziwa anthu onse. Onani mutuwo |