Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 3:1 - Buku Lopatulika

1 Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Munthu wina wa m'gulu la Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo panali Mfarisi wotchedwa Nekodimo, wa mʼgulu lolamulira la Ayuda.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 3:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,


Koma anadzanso Nikodemo, amene anadza kwa Iye usiku poyamba paja, alikutenga chisakanizo cha mure ndi aloe, monga miyeso zana.


Yesu anayankha nati kwa iye, Kodi uli mphunzitsi wa Israele, ndipo sudziwa izi?


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa