Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Mose adatenga ngolo ndi ng'ombe zija nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Mose anatenga ngolo ndi ngʼombe zothenazo nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo



Numeri 7:6
4 Mawu Ofanana  

Tsopano mwalamulidwa chitani ichi; muwatengere ana anu ndi akazi magaleta a m'dziko la Ejipito; nimubwere naye atate wanu.


Ndipo anagwetsa chihema; ndi ana a Geresoni, ndi ana a Merari, akunyamula chihema, anamuka nacho.


Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.


Anapatsa ana a Geresoni magaleta awiri ndi ng'ombe zinai, monga mwa ntchito yao;