Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:7 - Buku Lopatulika

7 Anapatsa ana a Geresoni magaleta awiri ndi ng'ombe zinai, monga mwa ntchito yao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Anapatsa ana a Geresoni magaleta awiri ndi ng'ombe zinai, monga mwa ntchito yao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ana a Geresoni adaŵapatsa ngolo ziŵiri ndi ng'ombe zinai potsata ntchito yao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Anapereka ngolo ziwiri ndi ngʼombe zothena zinayi kwa Ageresoni monga mwantchito yawo

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:7
4 Mawu Ofanana  

Tsopano mwalamulidwa chitani ichi; muwatengere ana anu ndi akazi magaleta a m'dziko la Ejipito; nimubwere naye atate wanu.


Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa