Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:8 - Buku Lopatulika

8 napatsa ana a Merari magaleta anai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu, monga mwa ntchito yao; wakuziyang'anira ndiye Itamara mwana wa Aroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 napatsa ana a Merari magaleta anai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu, monga mwa ntchito yao; wakuziyang'anira ndiye Itamara mwana wa Aroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ana a Merari adaŵapatsa ngolo zinai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu potsata ntchito yao, imene woyang'anira wake anali Itamara, mwana wa wansembe Aroni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 ndiponso anapereka ngolo zinayi ndi ngʼombe zothena zisanu ndi zitatu kwa Amerari molingananso ndi ntchito yawo. Onsewa ankawayangʼanira anali Itamara mwana wa Aaroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:8
3 Mawu Ofanana  

Tsopano mwalamulidwa chitani ichi; muwatengere ana anu ndi akazi magaleta a m'dziko la Ejipito; nimubwere naye atate wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa