Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 7:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 ndiponso anapereka ngolo zinayi ndi ngʼombe zothena zisanu ndi zitatu kwa Amerari molingananso ndi ntchito yawo. Onsewa ankawayangʼanira anali Itamara mwana wa Aaroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 napatsa ana a Merari magaleta anai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu, monga mwa ntchito yao; wakuziyang'anira ndiye Itamara mwana wa Aroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 napatsa ana a Merari magaleta anai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu, monga mwa ntchito yao; wakuziyang'anira ndiye Itamara mwana wa Aroni wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ana a Merari adaŵapatsa ngolo zinai ndi ng'ombe zisanu ndi zitatu potsata ntchito yao, imene woyang'anira wake anali Itamara, mwana wa wansembe Aroni.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:8
3 Mawu Ofanana  

“Uwawuzenso kuti, ‘Tengani ngolo zingapo za kuno ku Igupto kuti mukakwezepo ana anu, akazi anu pamodzi ndi abambo ako ndi kubwera nawo kuno.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa