Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Choncho Mose adatenga ngolo ndi ng'ombe zija nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Choncho Mose anatenga ngolo ndi ngʼombe zothenazo nazipereka kwa Alevi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:6
4 Mawu Ofanana  

Tsopano mwalamulidwa chitani ichi; muwatengere ana anu ndi akazi magaleta a m'dziko la Ejipito; nimubwere naye atate wanu.


Ndipo anagwetsa chihema; ndi ana a Geresoni, ndi ana a Merari, akunyamula chihema, anamuka nacho.


Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.


Anapatsa ana a Geresoni magaleta awiri ndi ng'ombe zinai, monga mwa ntchito yao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa