Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:32 - Buku Lopatulika

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso kambale kamodzi kagolide kolemera magaramu 110, kodzaza ndi lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;

Onani mutuwo



Numeri 7:32
7 Mawu Ofanana  

Ndidzakufukizirani nsembe zopsereza zonona, pamodzi ndi chofukiza cha mphongo za nkhosa; ndidzakonza ng'ombe pamodzi ndi mbuzi.


Pakuti kuyambira kotulukira dzuwa kufikira kolowera kwake dzina langa lidzakhala lalikulu mwa amitundu; ndipo m'malo monse adzaperekera dzina langa chofukiza ndi chopereka choona; pakuti dzina langa lidzakhala lalikulu mwa amitundu, ati Yehova wa makamu.


chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;


chopereka chake ndicho mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika, zonse ziwiri zodzaza ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;


ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;


Ndipo khamu lonse la anthu linalikupemphera kunja nthawi ya zonunkhira.


Ndipo anadza mngelo wina, naima paguwa la nsembe, nakhala nacho chotengera cha zofukiza chagolide; ndipo anampatsa zofukiza zambiri, kuti aziike pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima onse paguwa la nsembe lagolide, lokhala kumpando wachifumu.