Luka 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo khamu lonse la anthu linalikupemphera kunja nthawi ya zonunkhira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo khamu lonse la anthu linalikupemphera kunja nthawi ya zonunkhira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Khamu lonse la anthu linkapemphera kunja pa nthaŵi yofukiza lubaniyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo nthawi yofukiza lubani itafika, gulu lonse lopembedza linkapemphera kunja. Onani mutuwo |