Luka 1:9 - Buku Lopatulika9 monga mwa machitidwe a kupereka nsembe, adamgwera maere akufukiza zonunkhira polowa iye mu Kachisi wa Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 monga mwa machitidwe a kupereka nsembe, adamgwera maere akufukiza zonunkhira polowa iye m'Kachisi wa Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Potsata dongosolo lao la ansembe, iye adaasankhidwa mwamaere kuti akaloŵe m'Nyumba ya Mulungu kukafukiza lubani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Zakariyayo anasankhidwa mwa maere, monga mwa mwambo wa unsembe, kupita mʼNyumba ya Ambuye kukafukiza lubani. Onani mutuwo |