Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:22 - Buku Lopatulika

Werenganso ana a Geresoni, monga mwa nyumba za makolo ao, monga mwa mabanja ao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Werenganso ana a Geresoni, monga mwa nyumba za makolo ao, monga mwa mabanja ao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Uŵerengenso ana a Geresoni potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Werenganso Ageresoni monga mwa mabanja ndi mafuko awo.

Onani mutuwo



Numeri 4:22
5 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Geresoni maina ao ndi awa, monga mwa mabanja ao: Libini, ndi Simei.


Banja la Libini, ndi mabanja a Simei, ndiwo a Geresoni; ndiwo mabanja a Geresoni.


Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Uwawerenge kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu, kufikira a zaka makumi asanu; onse akulowa kutumikira utumikiwo, kuchita ntchitoyi m'chihema chokomanako.