Numeri 3:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Eliyasafu mwana wa Laele ndiye anali mtsogoleri wa banja la makolo a Ageresoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mtsogoleri wa mabanja a Ageresoni anali Eliyasafu mwana wa Laeli. Onani mutuwo |