Numeri 3:23 - Buku Lopatulika23 Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa chihema kumadzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa Kachisi kumadzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Mabanja a Geresoni ankamanga zithando zao kumbuyo kwa chihema cha Mulungu mbali yakuzambwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mabanja a Ageresoni azimanga misasa yawo kumadzulo, kumbuyo kwa Chihema. Onani mutuwo |