Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 3:23 - Buku Lopatulika

23 Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa chihema kumadzulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa Kachisi kumadzulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mabanja a Geresoni ankamanga zithando zao kumbuyo kwa chihema cha Mulungu mbali yakuzambwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Mabanja a Ageresoni azimanga misasa yawo kumadzulo, kumbuyo kwa Chihema.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 3:23
4 Mawu Ofanana  

Koma Alevi amange mahema ao pozungulira pa chihema cha mboni, kuti mkwiyo ungagwere khamu la ana a Israele; ndipo Alevi azidikira chihema cha mboni.


Pamenepo khamu la Alevi azimuka nacho chihema chokomanako, pakati pa makamu; monga amamanga mahema ao, momwemo azimuka ulendo wao, munthu yense pamalo pake, monga mwa mbendera zao.


Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.


Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa