Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:

Onani mutuwo



Numeri 4:1
6 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ndipo Ine, taona, ndampatsa Oholiyabu, mwana wa Ahisamaki, wa fuko la Dani, akhale naye; ndipo ndaika luso m'mitima ya onse a mtima waluso, kuti apange zonse ndakuuza iwe;


Koma adzakhala atumiki m'malo anga opatulika, akuyang'anira kuzipata za Kachisi, ndi kutumikira mu Kachisimo, aziwaphera anthu nsembe yopsereza, ndi nsembe yophera, naime pamaso pao kuwatumikira.


Ndipo akati amuke nacho chihemacho, Alevi amgwetse, ndipo akati achimange, Alevi achiimike; ndipo mlendo akayandikizako amuphe.


Ndipo Mose anapatsa Aroni ndi ana ake ndalama zoombola nazo monga mwa mau a Yehova, monga Yehova adauza Mose.


Werengani ana a Kohati pakati pa ana a Levi, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao,