Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 46:11 - Buku Lopatulika

11 Ndi ana aamuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndi ana amuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Ana a Levi anali aŵa: Geresoni, Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ana aamuna a Levi ndi awa: Geresoni, Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:11
17 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenganso pakati nabala mwana wamwamuna, nati, Tsopano lino mwamuna wanga adzadziphatika kwa ine chifukwa ndambalira iye ana aamuna atatu; chifukwa chake anamutcha dzina lake Levi.


Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani.


Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Israele ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuloni,


ndi Nasoni anabala Salimoni, ndi Salimoni anabala Bowazi,


ndi alongo ao ndiwo Zeruya ndi Abigaile. Ndi ana a Zeruya: Abisai ndi Yowabu, ndi Asahele; atatu.


Ana a Levi: Geresomo, Kohati ndi Merari.


Akulu a mbumba za makolo ao ndi awa: ana aamuna a Rubeni, woyamba wa Israele ndiwo: Hanoki ndi Palu, Hezironi, ndi Karimi; amenewo ndiwo mabanja a Rubeni.


Ndipo maina a ana aamuna a Levi, mwa kubadwa kwao ndiwo: Geresoni, ndi Kohati, ndi Merari; ndipo zaka za moyo wa Levi ndizo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa