Genesis 46:10 - Buku Lopatulika10 Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndi ana amuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ana a Simeoni anali aŵa: Yemuwele, Yamini, Ohadi, Yakini, Zohari ndi Shaulo, amene mai wake anali mkazi wa ku Kanani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ana aamuna a Simeoni ndi awa: Yemueli, Yamini, Ohadi, Yakini, Zohari ndi Shaulo amene mayi wake anali wa ku Kanaani. Onani mutuwo |