Genesis 46:9 - Buku Lopatulika9 Ndi ana aamuna a Rubeni: Hanoki, ndi Palu, ndi Hezironi, ndi Karimi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndi ana amuna a Rubeni: Hanoki, ndi Palu, ndi Hezironi, ndi Karimi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 ndi ana aŵa a Rubeni: Hanoki, Palu, Hezironi ndi Karimi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ana aamuna a Rubeni ndi awa: Hanoki, Palu, Hezironi ndi Karimi. Onani mutuwo |