Genesis 46:8 - Buku Lopatulika8 Maina a ana a Israele amene anadza mu Ejipito ndi awa: Yakobo ndi ana aamuna ake: Rubeni mwana wamwamuna woyamba wa Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Maina a ana a Israele amene anadza m'Ejipito ndi awa: Yakobo ndi ana amuna ake: Rubeni mwana wamwamuna woyamba wa Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Naŵa maina a Aisraele amene adapita ku Ejipito, ndiye kuti Yakobe ndi ana ake. Rubeni, mwana wachisamba wa Yakobe, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nawa ana a Israeli (ndiye kuti Yakobo ndi ana ake) amene anapita ku Igupto: Rubeni mwana woyamba wa Yakobo. Onani mutuwo |