Genesis 46:7 - Buku Lopatulika7 ana ake aamuna, ndi zidzukulu zake zazimuna, ndi ana aakazi ake, ndi zidzukulu zake zazikazi, ndi mbeu zake zonse anadza nazo mu Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ana ake amuna, ndi zidzukulu zake zazimuna, ndi ana akazi ake, ndi zidzukulu zake zazikazi, ndi mbeu zake zonse anadza nazo m'Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 ndiye kuti ana ndi adzukulu ake aamuna, ndiponso ana ndi adzukulu ake aakazi. Onsewo adapita nawo ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndiye kuti popita ku Igupto Yakobo anatenga ana aamuna, zidzukulu zazimuna, ana aakazi ndi zidzukulu zazikazi. Onani mutuwo |